-
2 Mafumu 23:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Yosiya atatembenuka nʼkuona manda amene anali paphiri, anauza anthu kuti akatenge mafupa mʼmandawo ndipo anawatentha paguwa lansembelo. Anachititsa guwalo kukhala losayenera kulambirapo, mogwirizana ndi mawu a Yehova amene munthu wa Mulungu woona uja ananena, yemwe analosera kuti zimenezi zidzachitika.+
-