Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 3:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Aisiraeli anayamba kugwetsa mizinda. Pamalo alionse abwino, aliyense anali kuponyapo mwala mpaka kudzaza malo onsewo. Anatseka kasupe aliyense wamadzi+ ndiponso kugwetsa mtengo uliwonse wabwino.+ Mpanda wamiyala wa mzinda wa Kiri-hareseti+ wokha ndi umene unatsala ndipo oponya miyala anazungulira mzindawo nʼkugwetsa mpandawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena