Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 6:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Elisa anali mʼnyumba mwake pamodzi ndi akulu. Mfumu inatumiza munthu kuti atsogole kupita kwa Elisa, koma munthuyo asanafike Elisa anauza akuluwo kuti: “Kodi mwaona kuti mwana wa munthu wopha anthu+ uja watumiza munthu kuti adzandidule mutu? Muonetsetse kuti munthuyo akangofika mutseke chitseko ndipo muchitsamire kuti asalowe. Kodi mapazi a mbuye wake si amene akumveka pambuyo pakewo?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena