-
2 Mafumu 9:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 Zitatero Yehu anakoka uta wake nʼkubaya Yehoramu kumsana pakati pamapewa mpaka muviwo unatulukira pamtima pake ndipo Yehoramu anagwa mʼgaleta lake lankhondo.
-