-
2 Mafumu 10:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Yehu atangomaliza kupereka nsembe yopserezayo, anauza asilikali ake othamanga ndi othandiza pamagaleta kuti: “Lowani muwaphe! Pasapezeke aliyense wothawira panja.”+ Choncho asilikali othamanga ndi othandiza pamagaletawo anayamba kupha anthuwo ndi lupanga nʼkumaponya mitembo yawo panja. Anakafika mpaka mʼchipinda chamkati* cha kachisi wa Baalayo.
-