-
2 Mafumu 11:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Atafika anaona mfumu itaimirira pafupi ndi chipilala mogwirizana ndi mwambo wawo.+ Atsogoleri a asilikali ndi anthu oimba malipenga+ anali ndi mfumuyo ndipo anthu onse amʼdzikolo ankasangalala komanso ankaimba malipenga. Ataliya ataona zimenezi anangʼamba zovala zake nʼkuyamba kukuwa kuti: “Mwandichitira chiwembu! Mwandichitira chiwembu!”
-