-
2 Mafumu 11:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Atatero anauza atsogoleri a magulu a asilikali 100,+ asilikali olondera mfumu a Chikariya, asilikali olondera nyumba yachifumu+ ndi anthu onse amʼdzikolo, kuti aperekeze mfumuyo kuchokera kunyumba ya Yehova. Anthuwo anafika kunyumba ya mfumu kudzera pageti la asilikali olondera kunyumba yachifumu. Kenako mfumuyo inakhala pampando wachifumu wa mafumu.+
-