-
1 Mbiri 9:33Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
33 Amenewa anali oimba, atsogoleri a nyumba za makolo a Alevi mʼzipinda zodyera. Iwo sankapatsidwa ntchito zina chifukwa ankagwira ntchito yawo masana komanso usiku.
-