-
1 Mbiri 12:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Anthu ena a fuko la Gadi anapita kumbali ya Davide pamene iye anali kumalo ovuta kufikako mʼchipululu.+ Amenewa anali asilikali amphamvu, ophunzitsidwa bwino nkhondo ndipo ankakhala okonzeka ndi zishango zawo zazikulu ndiponso mikondo yawo ingʼonoingʼono. Nkhope zawo zinali ngati za mikango ndipo anali aliwiro ngati mbawala mʼmapiri.
-