-
1 Mbiri 28:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Komabe, mʼnyumba yonse ya bambo anga Yehova Mulungu wa Isiraeli anasankha ineyo kuti ndikhale mfumu ya Isiraeli mpaka kalekale,+ chifukwa anasankha Yuda kuti akhale mtsogoleri.+ Mʼnyumba ya Yuda anasankhamo nyumba ya bambo anga.+ Pa ana a bambo anga anavomereza ineyo kuti ndikhale mfumu ya Aisiraeli onse.+
-