-
2 Mbiri 2:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Choncho nditumizireni munthu waluso pa ntchito za golide, siliva, kopa,*+ chitsulo, ubweya wapepo komanso za ulusi wofiira ndi wabuluu. Munthuyo akhalenso wodziwa kujambula ndi kulemba mochita kugoba. Azidzagwira ntchito ku Yuda ndi ku Yerusalemu limodzi ndi anthu anga aluso amene Davide bambo anga anawasankha.+
-