Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho nditumizireni munthu waluso pa ntchito za golide, siliva, kopa,*+ chitsulo, ubweya wapepo komanso za ulusi wofiira ndi wabuluu. Munthuyo akhalenso wodziwa kujambula ndi kulemba mochita kugoba. Azidzagwira ntchito ku Yuda ndi ku Yerusalemu limodzi ndi anthu anga aluso amene Davide bambo anga anawasankha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena