-
2 Mbiri 2:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Mayi ake ndi a fuko la Dani, koma bambo ake anali a ku Turo. Iye ndi wodziwa ntchito za golide, siliva, kopa, chitsulo, miyala, matabwa, ubweya wapepo, nsalu zabwino kwambiri komanso ulusi wabuluu ndi wofiira.+ Amathanso kujambula ndi kulemba mochita kugoba ndipo amadziwa kupanga chilichonse chimene angauzidwe.+ Iye azidzagwira ntchito limodzi ndi anthu anu aluso ndiponso anthu aluso a mbuye wanga Davide bambo anu.
-