-
2 Mbiri 8:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Anatsatira dongosolo la tsiku ndi tsiku loperekera nsembe mogwirizana ndi lamulo la Mose. Nsembezo zinali za pa Masabata,+ za pa masiku amene mwezi watsopano waoneka+ ndi za pa zikondwerero zomwe zinkachitika katatu pa chaka.+ Zikondwererozo zinali Chikondwerero cha Mikate Yopanda Zofufumitsa,+ Chikondwerero cha Masabata+ ndi Chikondwerero cha Misasa.+
-