Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 25:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako Amaziya anasonkhanitsa Ayuda nʼkuwauza kuti aime motsatira nyumba za makolo awo. Anawaika mʼmagulu a anthu 1,000 ndiponso mʼmagulu a anthu 100 limodzi ndi atsogoleri awo, a mafuko a Yuda ndi Benjamini.+ Iye anawalemba mayina anthuwo, kuyambira azaka 20 kupita mʼtsogolo+ ndipo anapeza kuti panali asilikali ophunzitsidwa bwino* komanso oyenera kupita kunkhondo okwana 300,000, oti angathe kunyamula mkondo waungʼono ndi chishango chachikulu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena