Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako amuna amene anachita kusankhidwa powatchula mayina ananyamuka nʼkutenga anthu ogwidwawo. Anthu onse amene sanavale* anawapatsa zovala kuchokera pa zinthu zimene zinabwera ndi asilikali zija. Anawapatsanso nsapato, chakudya, zakumwa komanso mafuta kuti adzole. Kuwonjezera pamenepo, aliyense amene ankayenda movutikira anamukweza pabulu. Atatero anawatenga nʼkupita nawo ku Yeriko, kumzinda wa mitengo ya kanjedza, kufupi ndi abale awo. Kenako iwo anabwerera ku Samariya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena