Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mʼchaka chachiwiri kuchokera pamene anabwera kunyumba ya Mulungu woona ku Yerusalemu, mʼmwezi wachiwiri, Zerubabele mwana wa Salatiyeli, Yesuwa mwana wa Yehozadaki, abale awo onse, ansembe ndi Alevi ndiponso anthu ena onse amene anabwera ku Yerusalemu kuchokera ku ukapolo,+ anayamba kugwira ntchito. Anasankha Alevi oyambira zaka 20 kupita mʼtsogolo kuti akhale oyangʼanira ntchito yapanyumba ya Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena