-
Nehemiya 1:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Chonde, tsegulani maso anu ndi kutchera khutu kuti mumve pemphero la ine mtumiki wanu limene ndikupemphera kwa inu lero. Masana ndi usiku+ ndikumapempherera atumiki anu, Aisiraeli. Pochita zimenezi ndikuvomereza machimo a Aisiraeli amene tinakuchimwirani. Tonse tinachimwa, ine limodzi ndi nyumba ya bambo anga.+
-