-
Nehemiya 7:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Koma Mulungu wanga anaika nzeru mumtima mwanga kuti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, atsogoleri ndi anthu onse kuti alembetse mayina motsatira mndandanda wa makolo awo.+ Ndiyeno ndinapeza buku la mndandanda wa mayina wa anthu amene anabwera moyambirira kuchokera ku ukapolo. Ndinapeza kuti mʼbukumo analembamo izi:
-