Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Panali makatani a nsalu zoyera, makatani opangidwa ndi thonje labwino kwambiri ndi makatani abuluu. Makataniwo anawamanga ndi zingwe zopangidwa ndi nsalu zabwino kwambiri ndipo anawapachika mʼmikombero yasiliva yokulungidwa ndi ulusi wapepo. Mikomberoyo anaikoleka pa zipilala za miyala ya mabo. Panalinso mipando yagolide ndi siliva yokhala ngati mabedi imene inali pakhonde la miyala ya pofeli,* miyala yoyera ya mabo, ngale ndi miyala yakuda ya mabo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena