Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anamupatsanso kalata imene munali lamulo lochokera ku Susani*+ loti Ayuda onse aphedwe. Anamupatsa kalatayi kuti akaonetse Esitere ndiponso akamufotokozere mmene zinthu zilili. Moredikayi anauzanso Hataki kuti akauze Esitere+ kuti akaonekere kwa mfumu nʼkupempha kuti imuchitire chifundo ndiponso kuti akachonderere mfumuyo pamasomʼpamaso mʼmalo mwa anthu a mtundu wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena