-
Yobu 5:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Chifukwa iye amapangitsa kuti munthu amve kupweteka, koma amamanga chilonda chopwetekacho.
Amaphwanya anthu, koma amawachiritsa ndi manja ake.
-