-
Mlaliki 9:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Anthu onse mapeto awo ndi ofanana,+ munthu wolungama komanso munthu woipa,+ munthu wabwino ndi woyera komanso munthu wodetsedwa, munthu amene amapereka nsembe komanso amene sapereka nsembe. Munthu wabwino nʼchimodzimodzi ndi munthu wochimwa. Munthu amene amachita lumbiro nʼchimodzimodzi ndi amene amaganiza kaye asanachite lumbiro.
-