Mlaliki 10:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Chakudya chimachititsa kuti anthu aziseka, ndipo vinyo amachititsa kuti moyo ukhale wosangalatsa,+ koma ndalama zimathandiza munthu kupeza chilichonse chimene akufuna.+ Mlaliki Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 10:19 Nsanja ya Olonda,5/15/1998, tsa. 4
19 Chakudya chimachititsa kuti anthu aziseka, ndipo vinyo amachititsa kuti moyo ukhale wosangalatsa,+ koma ndalama zimathandiza munthu kupeza chilichonse chimene akufuna.+