Yesaya 6:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Kenako ndinanena kuti: “Tsoka kwa ine! Maso anga aona Mfumu, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.Ndifa ine basi,Chifukwa ndine munthu wa milomo yodetsedwa,Ndipo ndikukhala pakati pa anthu a milomo yodetsedwa.”+ Yesaya Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 6:5 Yandikirani, ptsa. 32-34 Yesaya 1, ptsa. 90-92 Nsanja ya Olonda,4/1/1991, ptsa. 22-2310/15/1987, tsa. 16
5 Kenako ndinanena kuti: “Tsoka kwa ine! Maso anga aona Mfumu, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.Ndifa ine basi,Chifukwa ndine munthu wa milomo yodetsedwa,Ndipo ndikukhala pakati pa anthu a milomo yodetsedwa.”+
6:5 Yandikirani, ptsa. 32-34 Yesaya 1, ptsa. 90-92 Nsanja ya Olonda,4/1/1991, ptsa. 22-2310/15/1987, tsa. 16