-
Yesaya 8:22Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
22 Kenako adzayangʼana padziko lapansi ndipo adzangoonapo kuzunzika, mdima, kusowa mtengo wogwira, nthawi zovuta, mdima wandiweyani ndipo sadzaonapo kuwala.
-