Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 18:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Dzikolo limatumiza nthumwi zake kudzera panyanja,

      Zimadutsa pamadzi mʼngalawa zopangidwa ndi gumbwa.* Dzikolo limanena kuti:

      “Pitani, inu amithenga achangu,

      Ku mtundu wa anthu ataliatali komanso akhungu losalala,

      Kwa anthu amene kulikonse amaopedwa,+

      Kwa mtundu wa anthu amphamvu, amene akugonjetsa mitundu ina,

      Umene nthaka yake yakokoloka ndi mitsinje.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena