-
Yesaya 18:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Pa nthawi imeneyo, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzapatsidwa mphatso,
Kuchokera ku mtundu wa anthu ataliatali komanso akhungu losalala,
Kuchokera kwa anthu amene kulikonse amaopedwa,
Kuchokera kwa mtundu wa anthu amphamvu, amene akugonjetsa mitundu ina,
Umene nthaka yake yakokoloka ndi mitsinje.
Mphatsoyo adzaibweretsa kuphiri la Ziyoni, kumene kuli dzina la Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.”+
-