-
Yesaya 26:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Chifukwa taonani! Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala
Kuti adzaimbe mlandu anthu okhala mʼdzikoli chifukwa cha zolakwa zawo,
Ndipo dzikoli lidzaonetsa poyera magazi amene linakhetsa
Ndipo silidzabisanso anthu ake amene anaphedwa.”
-