-
Yesaya 37:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 Kudzera mwa atumiki ako, wanyoza Yehova+ ndipo wanena kuti,
‘Ndi magaleta anga ankhondo ambiri,
Ndidzakwera pamwamba pa mapiri,+
Ndidzafika kumadera akutali kwambiri a Lebanoni.
Ndidzadula mitengo yake ya mkungudza italiitali, ndi mitengo yake yabwino kwambiri ya junipa.*
Ndidzalowa kumalo ake amene ali pamwamba kwambiri, kunkhalango yowirira.
-