Yesaya 57:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Chifukwa ine sindidzatsutsana nawo mpaka kalekaleKapena kukhala wokwiya nthawi zonse.+Popeza mzimu wa munthu ukhoza kufooka chifukwa cha ine,+Ngakhale zinthu zopuma zimene ine ndinapanga. Yesaya Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 57:16 Yesaya 2, tsa. 271
16 Chifukwa ine sindidzatsutsana nawo mpaka kalekaleKapena kukhala wokwiya nthawi zonse.+Popeza mzimu wa munthu ukhoza kufooka chifukwa cha ine,+Ngakhale zinthu zopuma zimene ine ndinapanga.