-
Yesaya 61:3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Kuti ndisamalire anthu onse amene akulirira Ziyoni,
Kuti ndiwapatse nsalu yovala kumutu mʼmalo mwa phulusa,
Kuti ndiwapatse mafuta kuti azisangalala mʼmalo molira,
Kuti ndiwapatse chovala choti azivala ponditamanda mʼmalo mokhala otaya mtima.
-