Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 61:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kuti ndisamalire anthu onse amene akulirira Ziyoni,

      Kuti ndiwapatse nsalu yovala kumutu mʼmalo mwa phulusa,

      Kuti ndiwapatse mafuta kuti azisangalala mʼmalo molira,

      Kuti ndiwapatse chovala choti azivala ponditamanda mʼmalo mokhala otaya mtima.

      Ndipo iwo adzatchedwa mitengo ikuluikulu ya chilungamo,

      Yodzalidwa ndi Yehova kuti iyeyo alemekezedwe.*+

  • Yesaya
    Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
    • 61:3

      Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu,

      2/2017, tsa. 5

      Mapeto a Chivumbulutso, tsa. 312

      Yesaya 2, ptsa. 325-327

      Nsanja ya Olonda,

      10/1/1987, ptsa. 13-14

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena