5 Mwabwera kudzathandiza anthu amene amachita zinthu zolungama mosangalala,+
Anthu amene amakukumbukirani komanso kutsatira njira zanu.
Koma inu munakwiya chifukwa chakuti ifeyo tinkangopitiriza kuchimwa,+
Tinakhala tikuchimwa kwa nthawi yaitali.
Ndiye kodi panopa ndife oyenera kupulumutsidwa?