-
Yesaya 66:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Yehova adzapereka chiweruzo pogwiritsa ntchito moto,
Inde adzagwiritsa ntchito lupanga lake poweruza anthu onse,
Ndipo anthu ophedwa ndi Yehova adzakhala ambiri.
-