6 Iwo sanafunse kuti, ‘Ali kuti Yehova,
Amene anatitulutsa mʼdziko la Iguputo,+
Amene anatitsogolera mʼchipululu,
Mʼdziko la zipululu+ ndi mayenje,
Mʼdziko lachilala+ ndi lamdima wandiweyani,
Mʼdziko limene simudutsa munthu aliyense
Komanso mmene simukhala anthu?’