Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Uli ngati bulu wamʼtchire amene anazolowera kukhala mʼchipululu,

      Amene amanunkhiza pofunafuna amuna chifukwa cha chilakolako chake champhamvu.

      Ndi ndani amene angamubweze nthawi yoti akweredwe ikakwana?

      Abulu amphongo amene akumufunafuna sadzavutika kuti amupeze.

      Nyengo yoti* akweredwe ikakwana adzamupeza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena