-
Yeremiya 3:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Anthu amafunsa kuti: “Ngati mwamuna wathetsa ukwati ndi mkazi wake, ndipo mkaziyo akachokadi nʼkukakwatiwa ndi mwamuna wina, kodi mwamunayo angabwererenso kwa mkaziyo?”
Kodi dzikoli silaipitsidwa kale kwambiri?+
Yehova wanena kuti: “Iwe wachita uhule ndi amuna ambirimbiri.+
Ndiye kodi pano ukufuna ubwererenso kwa ine?
-