7 Mofanana ndi mkango umene ukutuluka paziyangoyango pamene umakhala,+
Amene akuwononga mitundu ya anthu wanyamuka.+
Wachoka mʼmalo ake kuti adzasandutse dziko lanu chinthu chochititsa mantha.
Mizinda yanu idzakhala mabwinja ndipo palibe munthu aliyense amene adzakhalemo.+