4 Kodi dzikoli likhalabe lofota mpaka liti?
Kodi zomera zamʼmunda uliwonse zikhalabe zouma mpaka liti?+
Chifukwa cha zinthu zoipa zimene anthu amʼdzikoli akuchita,
Zilombo zakutchire ndi mbalame zawonongedwa.
Chifukwa anthuwo akuti: “Iye sakuona zimene zidzatichitikire.”