15 Choncho Yehova wanena kuti: ‘Ponena za aneneri amene akulosera mʼdzina langa ngakhale kuti sindinawatume, amenenso akunena kuti lupanga kapena njala sizidzafika mʼdziko lino, ine ndikuti aneneri amenewo adzaphedwa ndi lupanga ndiponso njala yaikulu.+