19 Kodi Yuda mwamukaniratu, kapena kodi mukunyansidwa ndi Ziyoni?+
Nʼchifukwa chiyani mwatilanga chonchi moti sitingathenso kuchira?+
Timayembekezera mtendere, koma palibe chabwino chilichonse chimene chachitika.
Timayembekezera kuchiritsidwa, koma tikungoona zinthu zochititsa mantha.+