Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 20:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa ndinamva mphekesera zambiri zoipa.

      Zinthu zochititsa mantha zinali paliponse.+

      Iwo ankanena kuti, “Muimbeni mlandu, tiyeni timuimbe mlandu!”

      Munthu aliyense amene ankandifunira zabwino ankayembekezera kuti ndichite chinachake cholakwika.+

      Ankanena kuti: “Mwina alakwitsa chinachake ameneyu,

      Ndipo timugonjetsa nʼkumubwezera.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena