-
Yeremiya 20:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Iwo ankanena kuti, “Muimbeni mlandu, tiyeni timuimbe mlandu!”
Munthu aliyense amene ankandifunira zabwino ankayembekezera kuti ndichite chinachake cholakwika.+
Ankanena kuti: “Mwina alakwitsa chinachake ameneyu,
Ndipo timugonjetsa nʼkumubwezera.”
-