-
Yeremiya 25:30Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
30 Ndiyeno iweyo unenere mawu onsewa ndipo anthuwo uwauze kuti,
‘Yehova adzabangula ali kumwamba,
Ndipo adzachititsa kuti mawu ake amveke ali kumalo ake oyera kumene amakhala.
Iye adzabangula kwambiri polengeza chiweruzo chake kwa anthu amene akukhala mʼmalo ake.
Adzafuula mosangalala ngati anthu amene akuponda mphesa,
Adzaimba posonyeza kuti wapambana polimbana ndi anthu onse amene akukhala padziko lapansi.’
-