-
Yeremiya 27:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 ‘Choncho musamvere aneneri, anthu ochita zamaula, olota maloto, ochita zamatsenga ndi obwebweta amene ali pakati panu ndipo akukuuzani kuti: “Simudzatumikira mfumu ya Babulo.”
-