-
Yeremiya 37:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Kenako Mfumu Zedekiya inatuma anthu kuti akatenge Yeremiya.+ Atabwera naye, mfumuyo inamufunsa mafunso mwachinsinsi mʼnyumba mwake. Mfumuyo inamufunsa kuti: “Kodi pali mawu aliwonse ochokera kwa Yehova?” Yeremiya anayankha kuti: “Eya alipo!” Ndipo anapitiriza kuti: “Inuyo mudzaperekedwa mʼmanja mwa mfumu ya Babulo!”+
-