-
Yeremiya 42:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: ‘Mofanana ndi mmene ndinasonyezera anthu okhala mu Yerusalemu+ mkwiyo ndi ukali wanga, inunso ndidzakusonyezani mkwiyo wanga ngati mutapita ku Iguputo. Mudzakhala otembereredwa, chinthu chochititsa mantha, chinthu chonyozeka+ ndi chochititsa manyazi ndipo malo ano simudzawaonanso.’
-