-
Yeremiya 46:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 ‘Nʼchifukwa chiyani akuoneka kuti agwidwa ndi mantha?
Akubwerera ndipo asilikali awo agonjetsedwa.
Iwo athawa mwamantha ndipo asilikali awo sanacheuke.
Zochititsa mantha zili paliponse,’ akutero Yehova.
-