Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 46:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Limeneli ndi tsiku la Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa ndipo ndi tsiku lobwezera chilango kwa adani ake. Lupanga lidzadya adaniwo nʼkukhuta ndipo lidzamwa magazi awo mpaka ludzu lake litatha. Zimenezi zidzachitika chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa, ali ndi nsembe imene akufuna kupereka mʼdziko lakumpoto, mʼmphepete mwa mtsinje wa Firate.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena