-
Yeremiya 46:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 “Limeneli ndi tsiku la Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa ndipo ndi tsiku lobwezera chilango kwa adani ake. Lupanga lidzadya adaniwo nʼkukhuta ndipo lidzamwa magazi awo mpaka ludzu lake litatha. Zimenezi zidzachitika chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Ambuye Wamkulu Koposa, ali ndi nsembe imene akufuna kupereka mʼdziko lakumpoto, mʼmphepete mwa mtsinje wa Firate.+
-