12 Kwezani chizindikiro+ kuti muukire mpanda wa Babulo.
Wonjezerani alonda ndipo ikani alondawo pamalo awo.
Uzani omenya nkhondo mobisalira anzawo kuti akonzeke.
Chifukwa Yehova waganiza zoti achite,
Ndipo adzachitira anthu amene akukhala ku Babulo zimene ananena.”+