-
Yeremiya 51:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Ndidzakugwiritsa ntchito pophwanya mʼbusa ndi ziweto zake.
Ndidzakugwiritsa ntchito pophwanya mlimi ndi ziweto zimene amazigwiritsa ntchito polima.
Ndidzakugwiritsa ntchito pophwanya abwanamkubwa ndi achiwiri kwa olamulira.
-