-
Yeremiya 51:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 “Kwezani chizindikiro mʼdzikoli.+
Imbani lipenga pakati pa mitundu ya anthu.
Sankhani* mitundu ya anthu kuti ichite naye nkhondo.
Muitanireni maufumu a ku Ararati,+ ku Mini ndi ku Asikenazi+ kuti adzamuukire.
Muikireni wolemba anthu usilikali.
Mubweretsereni mahatchi ambiri ngati dzombe lingʼonolingʼono.
-